Psalms 119:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndikadakonda kuti njira zanga zikhale zokhulupirika, pakumvera malamulo anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ha? Mwenzi zitakhazikika njira zanga kuti ndisamalire malemba anu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Aa! Ndikanakonda njira zanga zikanakhala zokhazikika pa kumvera zophunzitsa zanu!
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ha! mwenzi zitakhazikika njira zanga Kuti ndisamalire malemba anu.