Psalms 119:51 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu osasamala za Mulungu amandinyoza kwathunthu, komabe sindisiyana nawo malamulo anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Odzikuza anandinyoza kwambiri: koma sindinapatukanso nacho chilamulo chanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Odzikuza amandinyoza popanda chowaletsa, koma sindichoka pa malamulo anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Odzikuza anandinyoza kwambiri: Koma sindinapatukanso naco cilamulo canu.