Psalms 119:52 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Inu Chauta, ndikamalingalira malamulo anu akalekale, ndimasangalala,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndinakumbukira maweruzo anu kuyambira kale, Yehova, ndipo ndinadzitonthoza.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndimakumbukira malamulo anu Yehova akalekale, ndipo mwa iwo ndimapeza chitonthozo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndinakumbukila maweruzo anu kuyambira kale, Yehova, Ndipo ndinadzitonthoza.