Psalms 119:53 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndimapsa mtima kwambiri chifukwa cha anthu oipa amene amaphwanya malamulo anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndinasumwa kwakukulu, chifukwa cha oipa akusiya chilamulo chanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndayipidwa kwambiri chifukwa cha oyipa amene ataya malamulo anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndinasumwa kwakukuru, Cifukwa ca oipa akusiya cilamulo canu.