Psalms 119:54 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Malamulo anu asanduka nyimbo yanga kulikonse kumene ndimapita.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Malemba anu anakhala nyimbo zanga m'nyumba ya ulendo wanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Zophunzitsa zanu ndi mitu ya nyimbo yanga kulikonse kumene ndigonako.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Malemba anu anakhala nyimbo zanga M'nyumba ya ulendo wanga,