Psalms 119:56 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Madalitso ameneŵa andifikira ine, pakuti ndimatsata malamulo anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ichi ndinali nacho, popeza ndinasunga malangizo anu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ichi ndicho ndakhala ndikuchita: ndimasunga malangizo anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ici ndinali naco, Popeza ndinasunga malangizo anu.