Psalms 119:58 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndikukupemphani ndi mtima wanga wonse, mundikomere mtima molingana ndi malonjezo anu aja.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndinapemba pankhope panu ndi mtima wanga wonse: Mundichitire chifundo monga mwa mau anu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndimafunafuna nkhope yanu ndi mtima wanga wonse; mundikomere mtima monga mwa lonjezo lanu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndinapemba pankhope panu ndi mtima wanga wonse: Mundicitire cifundo monga mwa mau anu.