Psalms 119:59 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndikamalingalira njira zanga, ndimatembenuka kuti nditsate malamulo anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndinaganizira njira zanga, ndipo ndinabweza mapazi anga atsate mboni zanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndinalingalira za njira zanga ndipo ndatembenuza mayendedwe anga kutsatira umboni wanu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndinaganizira njira zanga, Ndipo ndinabweza mapazi anga atsate mboni zanu.