Psalms 119:62 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndimadzuka pakati pa usiku kuti ndikutamandeni, chifukwa cha malangizo anu olungama.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakati pa usiku ndidzauka kukuyamikani chifukwa cha maweruzo anu olungama.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndimadzuka pakati pa usiku kuyamika Inu chifukwa cha malamulo anu olungama.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakati pa usiku ndidzauka kukuyamikani Cifukwa ca maweruzo anu olungama.