Psalms 119:7 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndidzakutamandani ndikuchita zoyenera, ndikaphunzira malangizo anu olungama.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndidzakuyamikani ndi mtima woongoka, pakuphunzira maweruzo anu olungama.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndidzakutamandani ndi mtima wolungama, pamene ndikuphunzira malamulo anu olungama.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndidzakuyanrikani ndi mtima woongoka, Pakuphunzira maweruzo anu olungama.