Psalms 119:70 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu otere ndi opulukira, koma ine ndimakondwa ndi malamulo anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mtima wao unona ngati mafuta; koma ine ndikondwera nacho chilamulo chanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mitima yawo ndi yowuma ndi yosakhudzidwa, koma ine ndimakondwera ndi malamulo anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mtima wao unona ngati mafuta; Koma ine ndikondwera naco cilamulo canu.