Psalms 119:71 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndi bwino kuti ndidalangidwa, kuti ndiphunzire malamulo anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kundikomera kuti ndinazunzidwa; kuti ndiphunzire malemba anu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndi bwino kuti ndinasautsidwa kuti ndithe kuphunzira malamulo anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kundikomera kuti ndinazunzidwa; Kuti ndiphunzire malemba anu.