Psalms 119:73 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Manja anu adandilenga ndi kundiwumba. Patseni nzeru zomvetsa, kuti ndiziphunzira malamulo anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Manja anu anandilenga nandiumba; mundizindikiritse, kuti ndiphunzire malemba anu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Manja anu anandilenga ndi kundiwumba; patseni nzeru zomvetsa zinthu kuti ndiphunzire malamulo anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Manja anu anandilenga nandiumba; Mundizindikiritse, kuti ndiphunzire malemba anu.