Psalms 119:74 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu okuwopani adzandiwona ndipo adzakondwa, popeza kuti ndakhulupirira mau anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Iwo amene akuopani adzandiona ine nadzakondwera; popeza ndayembekezera mau anu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwo amene amakuopani akondwere akandiona, chifukwa chiyembekezo changa chili mʼmawu anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Iwo amene akuopani adzandiona ine nadzakondwera; Popeza ndayembekezera mau anu;