Psalms 119:78 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu osasamala za Mulungu muŵachititse manyazi, chifukwa andilakwira pondinamizira. Koma ine ndidzasinkhasinkha za malamulo anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Odzikuza achite manyazi, popeza anandichitira monyenga ndi bodza: Koma ine ndidzalingalira malangizo anu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Odzikuza achititsidwe manyazi chifukwa cha kundilakwira popanda chifukwa; koma ine ndidzalingalira malangizo anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Odzikuza acite manyazi, popeza anandicitira monyenga ndi bodza: Koma ine ndidzalingalira malangizo anu.