Psalms 119:80 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mtima wanga ukhale wopanda choudzudzulira pa malamulo anu, kuti ndisachite manyazi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mtima wanga ukhale wangwiro m'malemba anu; kuti ndisachite manyazi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mtima wanga ukhale wopanda cholakwa pa chiphunzitso chanu kuti ndisachititsidwe manyazi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mtima wanga ukhale wangwiro m'malemba anu; Kuti ndisacite manyazi.