Psalms 119:81 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Moyo wanga wafooka podikira chipulumutso chanu, ndikukhulupirira mau anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Moyo wanga unakomoka ndi kukhumba chipulumutso chanu: Ndinayembekezera mau anu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Moyo wanga wafowoka ndi kufunafuna chipulumutso chanu, koma chiyembekezo changa chili mʼmawu anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Moyo wanga unakomoka ndi kukhumba cipulumutso canu: Ndinayembekezera mau anu.