Psalms 119:82 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Maso anga afiira nkuyang'anira malonjezo anu. Ndimafunsa kuti, “Kodi mudzandithandiza liti?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Maso anga anatha mphamvu ndi kukhumba mau anu, ndikuti, Mudzanditonthoza liti?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Maso anga alefuka pofunafuna lonjezo lanu; Ine ndikuti, “Kodi mudzanditonthoza liti?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Maso anga anatha mphamvu ndi kukhumba mau anu, Ndikuti, Mudzanditonthoza liti?