Psalms 119:84 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi mtumiki wanune ndipirire mpaka liti? Kodi anthu ondizunza mudzaŵalanga liti?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Masiku a mtumiki wanu ndiwo angati? Mudzaweruza liti iwo akundilondola koipa?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi mtumiki wanu ayenera kudikira mpaka liti? Kodi mudzawalanga liti amene amandizunza?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Masiku a mtumiki wanu ndiwo angati? Mudzaweruza liti iwo akundilondola koipa?