Psalms 119:86 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Malamulo anu onse ndi osasinthika. Anthuwo amandizunza ndi mabodza ao; thandizeni!
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Malamulo anu onse ngokhulupirika; andilondola nalo bodza; ndithandizeni.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Malamulo anu onse ndi odalirika; thandizeni, pakuti anthu akundizunza popanda chifukwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Malamulo anu onse ngokhulupirika; Andilondola nalo bodza; ndithandizeni.