Psalms 119:88 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Sungani moyo wanga chifukwa cha chikondi chanu chosasinthika, kuti nditsate malamulo anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mundipatse moyo monga mwa chifundo chanu; ndipo ndidzasamalira mboni ya pakamwa panu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Sungani moyo wanga molingana ndi chikondi chanu chosasinthika, ndipo ndidzamvera umboni wa pakamwa panu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mundipatse moyo monga mwa cifundo canu; Ndipo ndidzasamalira mboni ya pakamwa panu,