Psalms 119:9 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi mnyamata angathe bwanji kusunga makhalidwe ake kuti akhale angwiro? Akaŵasamala potsata mau anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mnyamata adzayeretsa mayendedwe ake bwanji? Akawasamalira monga mwa mau anu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi mnyamata angathe bwanji kuyeretsa mayendedwe ake? Akawasamala potsata mawu anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mnyamata adzayeretsa mayendedwe ace bwanji? Akawasamalira monga mwa mau anu.