Psalms 119:94 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndine wanu, pulumutseni, pakuti ndasamala malamulo anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ine ndine wanu, ndipulumutseni pakuti ndinafuna malangizo anu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndine wanu, ndipulumutseni; pakuti ndasamala malangizo anu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ine ndine wanu, ndipulumutseni Pakuti ndinafuna malangizo anu.