Psalms 119:95 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu oipa amandiŵenda kuti andiwononge, koma ine ndimalingalira za malamulo anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Oipa anandilalira kundiononga; koma ndizindikira mboni zanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu oyipa akudikira kuti andiwononge, koma ndidzalingalira umboni wanu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Oipa anandilalira kundiononga; Koma ndizindikira mboni zanu.