Psalms 119:96 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndazindikira kuti zabwino zonse zili ndi malire, koma malamulo anu alibe konse malire.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndinapenya malekezero ake a ungwiro wonse; koma lamulo lanu ndi lotakasuka ndithu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndadziwa kuti zinthu zonse zili ndi malire, koma malamulo anu alibe malire konse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndinapenya malekezero ace a ungwiro wonse; Koma lamulo lanu ndi lotakasuka ndithu.