Psalms 119:98 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Malamulo anu amandisandutsa wanzeru kuposa adani anga, popeza kuti malamulowo ndili nawo nthaŵi zonse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Malamulo anu andipatsa nzeru yakuposa adani anga; pakuti akhala nane chikhalire.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Malamulo anu amachititsa kuti ndikhale wanzeru kuposa adani anga, popeza malamulowo ali ndi ine nthawi zonse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Malamulo anu andipatsa nzeru yakuposa adani anga; Pakuti akhala nane cikhalire.