Psalms 119:99 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndili ndi nzeru za kumvetsa kupambana aphunzitsi anga onse, pakuti ndimasinkhasinkha za malamulo anu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndili nayo nzeru yakuposa aphunzitsi anga onse; pakuti ndilingalira mboni zanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndimamvetsa zinthu kwambiri kuposa aphunzitsi anga onse popeza ndimalingalira umboni wanu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndiri nayo nzeru yakuposa aphunzitsi anga onse; Pakuti ndilingalira mboni zanu.