Psalms 126:5 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu amene amafesa akulira, adzakolola akufuula ndi chimwemwe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Akubzala ndi misozi adzatuta ndi kufuula mokondwera.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwo amene amafesa akulira, adzakolola akuyimba nyimbo zachimwemwe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Akubzala ndi misozi adzatuta ndi kupfuula mokondwera.