Psalms 138:3 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pa tsiku limene ndidakuitanani, Inu mudandiyankha, mumandilimbitsa mtima ndi mphamvu zanu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Tsiku loitana ine, munandiyankha, munandilimbitsa ndi mphamvu m'moyo mwanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamene ndinayitana, munandiyankha; munandisandutsa wamphamvu ndi wolimba mtima.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Tsiku loitana ine, munandiyankha, Munandilimbitsa ndi mphamvu m'moyo mwanga.