Psalms 143:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndimatambalitsira manja anga kwa Inu, mtima wanga umamva ludzu lofuna Inu, monga limachitira dziko louma.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nditambalitsira manja anga kwa Inu: Moyo wanga ulira Inu monga dziko lolira mvula.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndatambalitsa manja anga kwa Inu; moyo wanga uli ndi ludzu lofuna Inu monga nthaka yowuma. Sela
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nditambalitsira manja anga kwa Inu: Moyo wanga ulira Inu monga dziko lolira mvula.