Psalms 143:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Lolani kuti m'maŵa ndimve za chikondi chanu chosasinthika, chifukwa ndimakhulupirira Inu. Mundisonyeze njira yoti ndiziyendamo, pakuti ndimapereka mtima wanga kwa Inu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mundimvetse chifundo chanu mamawa; popeza ndikhulupirira Inu: Mundidziwitse njira ndiyendemo; popeza ndikweza moyo wanga kwa Inu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Lolani kuti mmawa ubweretse mawu achikondi chanu chosasinthika, pakuti ine ndimadalira Inu. Mundisonyeze njira yoti ndiyendemo, pakuti kwa Inu nditukulira moyo wanga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mundimvetse cifundo canu mamawa; Popeza ndikhulupirira Inu: Mundidziwitse njira ndiyendemo; Popeza ndikweza moyo wanga kwa Inu.