Psalms 145:15 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Maso onse amayang'anira kwa Inu, ndipo mumaŵapatsa chakudya pa nthaŵi yake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Maso a onse ayembekeza Inu; ndipo muwapatsa chakudya chao m'nyengo zao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Maso a onse amayangʼana kwa Inu, ndipo Inu mumawapatsa chakudya chawo pa nthawi yoyenera.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Maso a onse ayembekeza Inu; Ndipo muwapatsa cakudya cao m'nyengo zao.