Psalms 145:5 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndidzasinkhasinkha za ulemerero ndi za ufumu wanu waukulu, ndidzalingalira za ntchito zanu zodabwitsa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndidzalingalira ulemerero waukulu wa ulemu wanu, ndi ntchito zanu zodabwitsa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Adzayankhula ulemerero wokongola waufumu wanu, ndipo ine ndidzalingalira za ntchito zanu zodabwitsa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndidzalingalira ulemerero waukuru wa ulemu wanu, Ndi nchito zanu zodabwiza.