Psalms 145:7 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adzasimba za ubwino wanu, adzaimba nyimbo zotamanda kulungama kwanu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Adzabukitsa chikumbukiro cha ubwino wanu waukulu, nadzaimbira chilungamo chanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Adzakondwerera kuchuluka kwa ubwino wanu, ndi kuyimba mwachimwemwe za chilungamo chanu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Adzabukitsa cikumbukilo ca ubwino wanu waukuru, Nadzayimbira cilungamo canu.