Psalms 146:1 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tamandani Chauta! Tamanda Chauta, iwe mtima wanga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Aleluya; Ulemekeze Yehova, moyo wanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tamandani Yehova. Tamanda Yehova, iwe moyo wanga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Haleluya; Ulemekeze Yehova, moyo wanga,