Psalms 146:9 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta amateteza alendo, amachirikiza mkazi wamasiye ndiponso mwana wamasiye. Koma njira za anthu oipa amazipotoza.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yehova asunga alendo; agwiriziza mwana wamasiye ndi mkazi wamasiye; koma akhotetsa njira ya oipa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova amasamalira alendo ndipo amathandiza ana ndi akazi amasiye, koma amasokoneza njira za anthu oyipa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yehova asunga alendo; Agwiriziza mwana wamasiye mkazi wamasiye; Koma akhotetsa njira ya oipa.