Psalms 28:6 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta atamandike, pakuti wamva liwu la kupempha kwanga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wodalitsika Yehova, Pakuti adamva mau a kupemba kwanga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Matamando apite kwa Yehova, popeza Iye wamva kupempha chifundo kwanga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wodalitsika Yehova, Pakuti adamva mau a kupemba kwanga.