Psalms 30:12 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Choncho ndisakhale chete, koma ndikutamandeni ndi mtima wonse. Choncho mtima wanga udzakuimbirani mosalekeza, Chauta, Mulungu wanga, ndidzakuthokozani mpaka muyaya.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
kuti ulemu wanga uimbire Inu, wosakhala chete. Yehova Mulungu wanga, ndidzakuyamikani nthawi zonse.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
kuti mtima wanga uthe kuyimbira Inu usakhale chete. Yehova Mulungu wanga, ndidzapereka kwa Inu mayamiko kwamuyaya.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kuti ulemu wanga uyimbire Inu, wosakhala cete. Yehova Mulungu wanga, ndidzakuyamikani nthawi zonse.