Psalms 33:10 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zolinga za anthu akunja Chauta amazisandutsa zopandapake. Maganizo ao onse amaŵasandutsa achabechabe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yehova aphwanya upo wa amitundu, asandutsa chabe zolingirira za mitundu ya anthu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova amalepheretsa chikonzero cha anthu a mitundu ina; Iye amaphwanya zolinga za anthu ambiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yehova aphwanya upo wa amitundu: Asandutsa cabe zolingirira za mitundu ya anthu.