Psalms 33:11 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma zolinga za Chauta zimachitika nthaŵi zonse, maganizo a mumtima mwake amakhazikika mpaka muyaya.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chiweruzo cha Yehova chikhazikika chikhazikikire, zolingirira za m'mtima mwake ku mibadwomibadwo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma chikonzero cha Yehova chimakhala mpaka muyaya, zolinga za mu mtima mwake pa mibado yonse.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ciweruzo ca Yehova cikhazikika cikhazikikire, Zolingirira za m'mtima mwace ku mibadwo mibadwo.