Psalms 34:13 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ngati ufunadi moyo, usalankhule zoipa, pakamwa pako pasakambe zonyenga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Uletse lilime lako lisatchule zoipa, ndipo milomo yako isalankhule chinyengo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
asunge lilime lake ku zoyipa ndi milomo yake kuti isayankhule zonama.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Uletse lilime lako lisachule zoipa, Ndipo milomo yako isalankhule cinyengo.