Psalms 34:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Yesani ndipo mudzaona kuti Chauta ndi wabwino. Ngwodala munthu wothaŵira kwa Chauta.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Talawani, ndipo onani kuti Yehova ndiye wabwino; wodala munthuyo wakukhulupirira Iye.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Lawani ndipo onani kuti Yehova ndi wabwino; wodala munthu amene amathawira kwa Iye.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Talawani, ndipo onani kuti Yehova ndiye wabwino; Wodala munthuyo wakukhulupirira Iye.