Psalms 44:19 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Komabe Inuyo mwatitswanya ndi kutisiya pakati pa nkhandwe ku chipululu, kumene kuli mdima wandiweyani.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
mungakhale munatithyola mokhala zilombo, ndi kutiphimba nao mthunzi wa imfa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma Inu mwatiphwanya ndi kuchititsa kuti tikhale ozunzidwa ndi ankhandwe ndipo mwatiphimba ndi mdima waukulu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mungakhale munatityola mokhala zirombo, Ndi kutiphimba nao mthunzi wa imfa.