Psalms 48:3 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mulungu waonetsa kuti ndiye woteteza mzindawo, pakuti Iye amakhala m'kati mwa malinga ake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mulungu adziwika m'zinyumba zake ngati msanje.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mulungu ali mu malinga ake; Iye wadzionetsa yekha kuti ndiye malinga akewo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mulungu adziwika m'zinyumba zace ngati msanje.