Psalms 51:5 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zoonadi, ndidabadwa mu uchimo, ndinali mu uchimo kuyambira pamene mai wanga adatenga pathupi pa ine.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Onani, ndinabadwa m'mphulupulu, ndipo mai wanga anandilandira m'zoipa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Zoonadi ine ndinali wochimwa pomwe ndimabadwa, wochimwa kuyambira pa nthawi imene amayi anga anakhala woyembekezera ine.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Onani, ndinabadwa m'mphulupulu: Ndipo mai wanga anandilandira m'zoipa.