Psalms 58:3 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu oipa ndi osokera kuyambira ali m'mimba mwa mai ao, anthu amabodza ndi otayika kuyambira tsiku la kubadwa kwao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Oipa achita chilendo chibadwire, asokera kuyambira kubadwa kwao, nanena bodza.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngakhale kuchokera tsiku lawo lobadwa oyipa amasochera; kuchokera mʼmimba ya amayi awo, iwo ndi otayika ndipo amayankhula mabodza.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Oipa acita cilendo cibadwire: Asokera kuyambira kubadwa kwao, nanena bodza.