Psalms 65:11 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pakutha pa chaka mumapereka zokolola zambiri mwa ubwino wanu, kulikonse kumene Inu mupita, kumapezeka dzinthu dzambiri.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Muveka chakachi ndi ukoma wanu; ndipo mabande anu akukha zakucha.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Inu mumaveka chaka ndi zinthu zochuluka, ndipo ngolo zanu zimasefukira ndi zinthu zochuluka.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mubveka cakaci ndi ukoma wanu; Ndipo mabande anu akukha zakuca.