Psalms 66:17 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndidafuula kwa Iye, ndipo ndidamtamanda ndi pakamwa panga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndinamfuulira Iye pakamwa panga, ndipo ndinamkuza ndi lilime langa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndinafuwula kwa Iye ndi pakamwa panga, matamando ake anali pa lilime panga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndinampfuulira Iye pakamwa panga, Ndipo ndinamkuza ndi lilime langa,