Psalms 67:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Inde, Mulungu watidalitsa, anthu onse a ku mathero a dziko lapansi apembedze Iye.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mulungu adzatidalitsa; ndipo malekezero onse a dziko lapansi adzamuopa Iye.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mulungu atidalitse kuti pamenepo malekezero onse a dziko lapansi apembedze Iyeyo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mulungu adzatidalitsa; Ndipo malekezero onse a dziko lapansi adzamuopa Iye,