Psalms 68:5 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Atate a ana amasiye ndiponso mtetezi wa azimai amasiye, ndi Mulungu amene amakhala m'malo ake oyera.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mulungu, mokhala mwake moyera, ndiye Atate wa ana amasiye, ndi woweruza wa akazi amasiye.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Atate wa ana amasiye, mtetezi wa akazi amasiye, ndiye Mulungu amene amakhala mʼmalo oyera.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mulungu, mokhala mwace mayera, Ndiye Atate wa ana amasiye, ndi woweruza wa akazi amasiye.